Masiku ndi Yesu

Tikupempherera kuti masiku ndi yesu akupatsani mwayi woona za mtima wake ndi m’mene afunira kuti mukhalire mutsogolere ndi kulimbikitsa ena. Tipiliza kupempemphera limodzi pamene pamene mukuyesetsa kupeleka moyo wanu, ubale wanu ndi utumiki wanu moganizilana ndi cholinga cha ufumu. Zikomo poyendera limodzi ndi yesu gulu la mentorlink.

Tsiku 1: Chiyambi  Genesis 1:1-26:5; Yesaya 52:7-53:12
Tsiku 2: Kubadwa kodabwitsa   Luka 1:3-2:18
Tsiku 3: Ubatizo wa Yesu   Luka 3:1-23
Tsiku 4: Satana akumuyesa Yesu   Luka 4:1-13
Tsiku 5: Utumiki wa yesu   Luka 4:16-31
Tsiku 6: Kudzichepetsa kweni kweni   Luka 18:10-14
Tsiku 7: Kugwira modabwitsa   Luka 5:4-11
Tsiku 8: Kuukitsa akufa   Luka 8:41-56
Tsiku 9: Kusankha khumi ndi awiri   Luka 5:27-28, 6:12-16
Tsiku 10: Madalitso   Luka 6:17-23
Tsiku 11: Uthenga wa pa phiri (part1)   Luka 6:24-42
Tsiku 12: Uthenga wa pa phiri (part 2)   Luka 6:24-42
Tsiku 13: Kukhululukidwa ndi kudzudzulidwa   Luka 7:36-50
Tsiku 14: Ophunziraakazi   Luka 8:1-3
Tsiku 15: Mafunso a Yohane   Luka 3:19-20;7:18-23
Tsiku 16: Fanizo la dothi   Luka 8:4-15
Tsiku 17: Fanizo la nyali   Luka 8:16-21
Tsiku 18: Mphepo ya mkuntho   Luka 8:22-26
Tsiku 19: Mizimu yoipa   Luka 8:27-39
Tsiku 20: Kudyetsa 5,000   Luka 9:11-17
Tsiku 21: Umwini wa yesu    Luka 9:18, 22 28-36
Tsiku 22: Pemphero la ambuye   Luka 11:1-4
Tsiku 23: Pemphero ndi nkhawa   Luka 11:9-13, 12:22-28; 17:6
Tsiku 24: Anthu aufumu   Luka 5:30-32; 17:1-2; 13:18-19
Tsiku 25: Kusemphana pa zaufumu   Luka 12:32-34; 13:10-17
Tsiku 26: Msamaria wabwino   Luka 10:25-37
Tsiku 27: Bambo osaona   Luka 18:35-43
Tsiku 28: Zakeyu   Luka 19:1-10
Tsiku 29: Kulowa mogonjetsa   Luka 18:31-34; 19:28-41
Tsiku 30: Za ndalama   Luka 19:45-48; 21:1-4
Tsiku 31: Ulamuliro wa Yesu   Luka 20:1-26
Tsiku 32: Mgonero womaliza    Luka 22:7-23
Tsiku 33: Chipinda cha pamwamba    Luka 22:26-38
Tsiku 34: Kugulitsidwa   Luka 22:40-65
Tsiku 35: Kufunsidwa   Luka 22:63-23:11
Tsiku 36: Kupachikida   Luka 23:26-38
Tsiku 37: Imfa ya Yesu    Luka 23:39-59
Tsiku 38: Wauka   Luka 23:56-24:50
Tsiku 39: Kuitanidwa   Aroma 3:23, 5:8, 6:23
Tsiku 40: Lamulo lalikulu   Mateyu 28:18-20